Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 3:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anakhazika guwa la nsembe patsinde pace cifukwa ca kuopa iwo anthu a m'maikomo; nakwezera Yehova nsembe zopsereza pamenepo, nsembe zopsereza zam'mawa ndi zamadzulo.

Werengani mutu wathunthu Ezara 3

Onani Ezara 3:3 nkhani