Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 10:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi kuti ali yense wosafikako atapita masiku atatu, monga mwa uphungu wa akalonga ndi akuru, cuma cace conse cidzaonongeka konse, ndipo iye adzacotsedwa ku msonkhano wa iwo otengedwa ndende.

Werengani mutu wathunthu Ezara 10

Onani Ezara 10:8 nkhani