Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Estere 7:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ninyamuka mfumu mu mkwiyo wace ku madyerero a vinyo, nimka ku munda wa maluwa wa kucinyumba; koma Hamani anatsalira kudzipempherera moyo kwa mkazi wamkuru Estere; popeza anapenya kuti mfumu inatsimikiza mtima kumcitira coipa.

Werengani mutu wathunthu Estere 7

Onani Estere 7:7 nkhani