Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 8:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsiku ilo ndidzalemba malire dziko la Goseni, m'mene mukhala anthu anga, kuti pamenepo pasakhale mizaza; kotero kuti udziwe kuti Ine ndine Yehova pakati pa dzikoli.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 8

Onani Eksodo 8:22 nkhani