Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 5:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwo anati, Mulungu wa Ahebri wakomana ndi ife; timuketu ulendo wa masiku atatu m'cipululu, kumphera nsembe Yehova Mulungu wathu; kuti angatikumike ndi mliri, kapena ndi lupanga,

Werengani mutu wathunthu Eksodo 5

Onani Eksodo 5:3 nkhani