Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 5:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Farao anati, Yehova ndani, kuti ndimvere mau ace ndi kulola Israyeli apite? Sindimdziwa Yehova, ndiponso sindidzalola Israyeli apite.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 5

Onani Eksodo 5:2 nkhani