Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 5:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anapanda akapitao a ana a Israyeli, amene ofulumiza a Farao adawaika, ndi kuti, Nanga dzulo ndi lero simunatsiriza bwanji nchito yanu yoneneka ya njerwa, monga kale?

Werengani mutu wathunthu Eksodo 5

Onani Eksodo 5:14 nkhani