Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 4:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, Pakumuka iwe kubwerera kumka ku Aigupto, usamalire ucite zozizwa zonse ndaziika m'dzanja lako, pamaso pa Farao; koma Ine ndidzalimbitsa mtima wace kuti asadzalole anthu kupita.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 4

Onani Eksodo 4:21 nkhani