Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 4:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Yehova ananena naye, Anampangira munthu m'kamwa ndani? Kapena analenga munthu wosalankhula ndani, kapena wogontha, kapena wamaso, kapena wakhungu? Si ndine Yehova kodi?

Werengani mutu wathunthu Eksodo 4

Onani Eksodo 4:11 nkhani