Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 39:35-39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

35. likasa la mboni, ndi mphiko zace, ndi cotetezerapo;

36. gomelo, zipangizo zace zonse, ndi mkate woonekera;

37. coikapo nyali coona, nyali zace, ndizo nyali zimakonzekazi, ndi zipangizo zace zonse, ndi mafuta a kuunikira;

38. ndi guwa la nsembe lagolidi, ndi mafuta odzoza, ndi cofukiza ca pfungo lokoma, ndi nsaru yotsekera pa khomo la cihemaco;

39. guwa la nsembe lamkuwa, ndi made ace amkuwa, mphiko zace, ndi zipangizo zace zonse, mkhate ndi tsinde lace;

Werengani mutu wathunthu Eksodo 39