Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 38:11-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Ndi pa mbali ya kumpoto mikono zana limodzi, nsici zace makumi awiri, nw makamwa ace makumi awiri, amkuwa; zokowera za nsici ndi mitanda yace yasiliva.

12. Ndi pa mbali ya kumadzulo panali nsaru zocingira za mikono makumi asanu, nsid zace khumi, ndi makamwa ace khumi; zokowera za nsici ndi mitanda yace yasiliva.

13. Ndi pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mikono makumi asanu.

14. Nsaru zocingira za pa mbali imodzi ya cipata nza mikono khumi ndi isanu; nsici zace zitatu, ndi makamwa ace atatu;

Werengani mutu wathunthu Eksodo 38