Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 37:10-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Ndipo anapanga gome la mtengo wasitimu; utali wace mikono iwiri, ndi kupingasa kwace mkono limodzi, ndi msinkhu wace mkono ndi hafu;

11. ndipo analikuta ndi golidi woona, nalipangira mkombero wagolidi pozungulira pace.

12. Analipangiranso mitanda pozungulirapo, yoyesa cikhato m'kupingasa kwace, ndi pamitanda pace pozungulira anapangirapo mkombero wagolidi.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 37