Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 36:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mose analamulira, ndipo anamveketsa mau mwa cigono conse, ndi kuti, Asaonjezere nchito ya ku copereka ca malo opatulika, ngakhale mwamuna ngakhale mkazi. Tero anawaletsa anthu asabwere nazo zina.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 36

Onani Eksodo 36:6 nkhani