Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 36:20-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. Ndipo anapanga matabwa a kacisi, oimirika, a mtengo wasitimu.

21. Utali wace wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwace kwa thabwa limodzi ndiko mkono ndi hafu.

22. Pa thabwa limodzi panakhala mitsukwa iwiri, yomangika pamodzi; anawapanga momwemo matabwa onse a kacisi.

23. Ndipo anapanga matabwa a kacisi; matabwa makumi awiri a ku mbali ya kumwela, kumwela;

Werengani mutu wathunthu Eksodo 36