Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 35:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Amuna ndi akazi onse a ana a Israyeli amene mitima yao inawafunitsa eni kubwera nazo za ku nchito yonse imene Yehova anauza Ipangike ndi dzanja la Mose, anabwera naco copereka cofuna mwini, kucipereka kwa Yehova.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 35

Onani Eksodo 35:29 nkhani