Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 33:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova ananena ndi Mose kopenyana maso, monga munthu alankhula ndi bwenzi lace. Ndipo anabwerera kumka kucigono; koma mtumiki wace Yoswa, mwana wa Nuni, ndiye mnyamata msinkhu wace, sanacoka m'cihemamo.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 33

Onani Eksodo 33:11 nkhani