Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 29:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adye zimene anacita nazo coteteza, kuti awadzaze manja ndi kuwapatulitsa; koma mlendo asadyeko, pakuti nzopatulika izi.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 29

Onani Eksodo 29:33 nkhani