Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 26:21-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.

22. Ndipo uzipanga matabwa asanu ndi limodzi kwa mbali ya kacisi ya kumbuyo kumadzulo.

23. Nupange matabwa awiri a ngondya za kacisi za kumbuyo.

24. Ndipo akhale ophatikizika pamodzi patsinde, nakhalenso ophatikizika pamodzi kumutu kwace ndi mphete imodzi; azitero onse awiri; azikhala a ngondya ziwiri.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 26