Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 19:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anati kwa Mose, Taona, ndikudza kwa iwe mu mtambo wakuda bii, kuti anthu amve pamene ndilankhula ndi iwe, ndi kuti akubvomereze nthawi zonse. Pakuti Mose adauza Yehova mau a anthuwo.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 19

Onani Eksodo 19:9 nkhani