Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 17:13-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. Ndipo Yoswa anatyola Amaleki ndi anthu ace ndi kuukali kwa lupanga.

14. Ndipo Yehova anati kwa Mose, Lembera ici m'buku, cikhale cikumbutso, nucimvetse Yoswa; kuti ndidzafafaniza konse cikumbukilo ca Amaleki pansi pa thambo.

15. Ndipo Mose anamanga guwa la nsembe, nalicha dzina lace Yehova Nisi:

16. nati, Yehova walumbira: padzakhala nkhondo ya Yehova pa Amaleki m'mibadwo mibadwo.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 17