Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 17:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma manja a Mose analema; ndipo anatenga mwala, nauika pansi pa iye, nakhala pamenepo; ndipo Aroni ndi Huri anagwiriziza manja ace, wina mbali yina, wina mbali yina; ndi manja ace analimbika kufikira litalowa dzuwa.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 17

Onani Eksodo 17:12 nkhani