Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 16:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anati kwa Mose, Taona, ndidzabvumbitsira inu mkate wodzera kumwamba; ndipo anthu azituruka ndi kuola muyeso wa tsiku pa tsiku lace, kuti ndiwayese, ngati ayenda m'cilamulo canga kapena iai.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 16

Onani Eksodo 16:4 nkhani