Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 16:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Taonani, popeza Yehova anakupatsani Sabata, cifukwa cace tsiku lacisanu ndi cimodzi alikupatsa inu mkate wofikira masiku awiri; khalani yense m'malo mwace, munthu asaturuke m'malo mwace tsiku lacisanu ndi ciwiri.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 16

Onani Eksodo 16:29 nkhani