Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 15:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti akavalo a Farao analowa m'nyanja, ndi magareta ace ndi apakavalo ace, ndipo Yehova anawabwezera madzi a m'nyanja; koma ana a Israyeli anayenda pouma pakati pa nyanja.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 15

Onani Eksodo 15:19 nkhani