Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 14:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Popeza madziwo anabwerera, namiza magareta ndi apakavalo, ndiwo nkhondo yonse ya Farao imene idalowa pambuyo pao m'nyanja; sanatsala wa iwowa ndi mmodzi yense.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 14

Onani Eksodo 14:28 nkhani