Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 14:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati kwa Mose, Kodi mwaticotsera kuti tikafe m'cipululu cifukwa panahbe manda m'Aigupto? Nciani ici mwaticitira kuti mwatiturutsa m'Aigupto?

Werengani mutu wathunthu Eksodo 14

Onani Eksodo 14:11 nkhani