Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 13:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi kuti,

2. Ndipatulire Ine yense woyamba kubadwa, wotsegulira pa amace mwa ana a Israyeli, mwa anthu ndi mwa zoweta; ndiwo anga.

3. Ndipo Mose ananena ndi anthu, Kumbukirani tsiku linu limene munaturuka m'Aigupto, m'nyumba ya akapolo; pakuti Yehova anakuturutsani muno ndi dzanja lamphamvu; ndipo asadye kanthu ka cotupitsa.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 13