Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 12:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ndidzapita pakati pa dziko la Aigupto usiku womwewo, ndi kukantha ana oyamba onse m'dziko la Aigupto, anthu ndi zoweta; ndipo ndidzacita maweruzo pa milungu yonse ya Aigupto; Ine ndine Yehova.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 12

Onani Eksodo 12:12 nkhani