Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 11:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anyamata ako onse awa adzanditsikira, nadzandigwadira, ndi kuti, Turukani inu, ndi anthu onse akukutsatani; ndipo pambuyo pace ndidzaturuka. Ndipo anaturuka kwa Farao wakupsa mtima.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 11

Onani Eksodo 11:8 nkhani