Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 4:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cokhaci, dzicenjerani nokha, ndi kusunga moyo wanu mwacangu, kuti mungaiwale zinthuzi adaziona maso anu, ndi kuti zisacoke kumtima kwanu masiku onse a moyo wanu; koma muzidziwitsa ana anu ndi zidzukulu zanu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 4

Onani Deuteronomo 4:9 nkhani