Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 31:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mose anaitana Yoswa, nati naye pamaso pa Israyeli wonse, Khala wamphamvu, nulimbe mtima; pakuti udzalowa nao anthu awa m'dziko limene Yehova analumbirira makolo ao kuwapatsa ilo; ndipo iwe udzawalandiritsa ilo.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 31

Onani Deuteronomo 31:7 nkhani