Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 31:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzakhala, zitawafikira zoipa ndi zobvuta zambiri, nyimbo iyi idzacita mboni pamaso pao; popeza siidzaiwalika m'kamwa mwa mbeu zao; popeza ndidziwa zolingirira zao azicita lero lino, ndisanawalowetse m'dziko limene ndinalumbira.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 31

Onani Deuteronomo 31:21 nkhani