Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 31:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano mudzilemberere nyimbo iyi, ndi kuphunzitsa ana a Israyeli iyi: mulike m'kamwa mwao, kuti nyimbo iyi indicitire mboni yotsutsa ana a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 31

Onani Deuteronomo 31:19 nkhani