Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:68 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova adzakubwezerani ku Aigupto ndi ngalawa, pa njira imene ndinati kwa inu, kuti, Simudzaionanso; ndipo kumeneko mudzadzigulitsa kwa adani anu mukhale akapolo ndi adzakazi; koma palibe wogulainu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:68 nkhani