Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:48 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

cifukwa cace mudzatumikira adani anu amene Yehova adzakutumizirani, ndi njala, ndi ludzu, ndi usiwa, ndi kusowa zinthu zonse; ndipo adzaika goli lacitsulo pakhosi panu, kufikira atakuonongani.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:48 nkhani