Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova adzakucurukitsirani zokoma, m'zipatso za thupi lanu, ndi m'zipatso za zoweta zanu, ndi m'zipatso za nthaka yanu, m'dziko limene Yehova analumbirira makolo anu kuti adzakupatsani ilo,

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:11 nkhani