Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 27:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo mulemberepo mau onse a cilamulo ici, mutaoloka; kuti mulowe m'dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani, dziko moyenda mkaka ndi uci ngati madzi, monga Yehova Mulungu wa makolo anu ananena ndi inu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 27

Onani Deuteronomo 27:3 nkhani