Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 24:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo akamuda mwamuna waciwiriyo, nakamlemberanso kalata wa cilekanitso, ndi kumpereka uyu m'dzanja lace, nakamturutsa m'nyumba mwace; kapena akamwalira mwamuna wotsirizayo, amene anamtenga akhale mkazi wace;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 24

Onani Deuteronomo 24:3 nkhani