Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 21:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Akapeza munthu waphedwa m'dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani likhale lanu lanu, nagona pamunda, wosadziwika wakumkantha,

2. pamenepo azituruka akuru anu ndi oweruza anu, nayese ku midzi yomzinga wophedwayo;

3. ndipo kudzali kuti mudzi wakukhala kufupi kwa munthu wophedwayo, inde akuru a mudzi uwu atenge ng'ombe yamsoti yosagwira nchito, yosakoka goli;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 21