Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 20:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mitengo yoidziwa inu kuti si ndiyo mitengo yazipatso, imeneyi muiononge ndi kuilikha; ndipo mudzi wocita nanu nkhondo muumangire macemba, mpaka mukaugonjetsa.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 20

Onani Deuteronomo 20:20 nkhani