Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 17:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Musamaphera Yehova Mulungu wanu nsembe ya ng'ombe, kapena nkhosa, yokhala naco cirema, kapena ciri conse coipa; pakuti cinyansira Yehova Mulungu wanu.

2. Akapeza pakati panu, m'mudzi wanu wina umene anakupatsani Yehova Mulungu wanu, wamwamuna kapena wamkazi wakucita ciri coipa pamaso pa Yehova Mulungu wanu, ndi kulakwira cipangano cace,

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 17