Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 16:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mukondwere pamaso pa Yehova Mulungu wanu, inu ndi ana anu amuna, ndi ana anu akazi, ndi anchito anu amuna, ndi anchito anu akazi, ndi Mlevi wokhala m'mudzi mwanu, ndi mlendo, ndi mwana wamasiye, ndi mkazi wamasiye, okhala pakati pa inu, m'malo amene Yehova Mulungu wanu adzasankha kukhalitsako dzina lace.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 16

Onani Deuteronomo 16:11 nkhani