Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 15:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mukagula mbale wanu, Mhebri wamwamuna kapena Mhebri wamkazi, ndipo adzakutumikira zaka zisanu ndi cimodzi; koma caka cacisanu ndi ciwiri umlole acoke kwanu waufulu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 15

Onani Deuteronomo 15:12 nkhani