Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 13:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mbale wanu, ndiye mwana wa mai wanu, kapena mwana wanu wamwamuna, kapena mwana wanu wamkazi, kapena mkazi wa kumtima kwanu, kapena bwenzi lanu, ndiye ngati moyo wanu wanu, akakukakamizani m'tseri, ndi kuti, Tipite titumikire milungu yina, imene simunaidziwa, inu, kapena makolo anu;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 13

Onani Deuteronomo 13:6 nkhani