Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 11:30-32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

30. Sakhala kodi tsidya lija la Yordano, m'tseri mwace mwa njira yace yolowa dzuwa, m'dziko la Akanani, akukhala m'cidikha, pandunji pace pa Giligala, pafupi pa mathunda a More?

31. Pakuti mulinkuoloka Yordano kulowa ndi kulandira dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani; ndipo mudzacilandira colowa canu, ndi kukhalamo.

32. Potero samalirani kucita malemba ndi maweruzo onse ndiwaika pamaso panu lero lino.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 11