Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 9:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

inde pakunena ine m'kupemphera, munthu uja Gabrieli, amene ndidamuona m'masomphenya poyamba paja, anauluka mwaliwiro nandikhudza ngati nthawi yakupereka nsembe ya madzulo.

Werengani mutu wathunthu Danieli 9

Onani Danieli 9:21 nkhani