Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 8:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tondeyo anadzikulitsa kwakukuru, koma atakhala wamphamvu, nyanga yace yaikuru inatyoka; ndi m'malo mwace munaphuka nyanga zinai zooneka bwino, zoloza ku mphepo zinai za mlengalenga.

Werengani mutu wathunthu Danieli 8

Onani Danieli 8:8 nkhani