Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 7:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndinali kulingirira za nyangazi, taonani, pakati pa izo panaphuka nyanga yina, ndiyo yaing'ono; patsogolo pace zitatu za nyanga zoyambazi zinazulidwa ndi mizu yomwe; ndipo taonani, m'nyanga m'menemo munali maso ngati maso a munthu, ndi pakamwa palikunena zazikuru.

Werengani mutu wathunthu Danieli 7

Onani Danieli 7:8 nkhani