Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 5:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo analowa naye Danieli kwa mfumu. Mfumu inayankha, niti kwa Danieli, Ndiwe kodi Danieli uja wa ana a ndende a Yuda, amene mfumu atate wanga anatenga ku Yuda?

Werengani mutu wathunthu Danieli 5

Onani Danieli 5:13 nkhani