Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 4:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Belitsazara iwe, mkuru wa alembi, popeza ndidziwa kuti mwa iwe muli mzimu wa milungu yoyera, ndi kuti palibe cinsinsi cikusautsa, undifotokozere masomphenya a loto langa ndalotali, ndi kumasulira kwace.

Werengani mutu wathunthu Danieli 4

Onani Danieli 4:9 nkhani